Ndege Za Shepherd Bushiri Ndi Chuma China Chodabwisa Zinapita Kuti ?
Автор: Hanifa Mw
Загружено: 2022-07-03
Просмотров: 169744
Описание:
NDEGE ZA BUSHIRI ZINAPITA KUTI?
A Shepherd Bushiri ndi mtsogoleri komanso mwini wa mpingo wina omwe umadziwika ndi dzina loti Enlightened Christian Gathering (ECG).
Kamba kakupanga zinthu zozizwitsa ndi zodabwitsa pa moyo wawo wolalika komanso ndi moyo wawo wokonda zinthu zodula zomwe zambiri ndi zapamwamba kwambiir, anthu ambiri amawadziwa makamaka chigawo chino cha Africa.
Iwo ndi mwana wa Prophet Uebert Angel mu uzimu (spiritual son) yemwe amakhala mdziko la United Kingdom (UK) ndipo zimamveka kuti ndi mmodzi mwa anthu olalika omwe ndi olemera kwambiri muno mu dera la Africa.
Kuyambira mchaka cha 2015, a Bushiri akhala akukumana ndi zinthu zomwe zakhala zikuwoneka kuti zikhoza kusokoneza utumiki wawo koma pa 1 February mu chaka cha 2019, iwo pamodzi ndi mkazi wawo Mary yemwe amatinso ndi mneneri ngati amuna awo, anamangidwa.
Повторяем попытку...
Доступные форматы для скачивания:
Скачать видео
-
Информация по загрузке: